Eksodo 8:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo tsiku ilo ndidzalemba malire dziko la Goseni, m'mene mukhala anthu anga, kuti pamenepo pasakhale mizaza; kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova pakati padzikoli. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo tsiku ilo ndidzalemba malire dziko la Goseni, m'mene mukhala anthu anga, kuti pamenepo pasakhale mizaza; kotero kuti udziwe kuti Ine ndine Yehova pakati pa dzikoli. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Pa tsiku limenelo ndidzapatula dziko la Goseni lokhalamo anthu anga, mwakuti lokhalo lidzakhala lopanda mizaza, kuti iweyo udziŵe kuti Ine ndine Chauta ndipo kuti ndikulamulira pa dziko lapansi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “Koma pa tsikulo ndidzapatula dera la Goseni, kumene kumakhala anthu anga, motero kuti sikudzakhala ntchentche zoluma. Choncho iwe udzadziwa kuti Ine Yehova ndi amene ndikulamulira dziko lino. Onani mutuwo |