Eksodo 8:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo achule adzachokera inu, ndi nyumba zanu, ndi anyamata anu, ndi anthu anu; adzatsala m'mtsinje mokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo achule adzachokera inu, ndi nyumba zanu, ndi anyamata anu, ndi anthu anu; adzatsala m'nyanja mokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Achulewo adzakuchokani, adzachokanso m'nyumba zanu, m'nyumba za nduna zanu, ndipo azidzangokhala mumtsinje mokha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Achule adzachoka mʼnyumba yanu, mʼnyumba za nduna zanu pamodzi ndi za anthu anu. Koma adzatsala mu mtsinje wa Nailo basi.” Onani mutuwo |