Eksodo 8:11 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Achule adzachoka mʼnyumba yanu, mʼnyumba za nduna zanu pamodzi ndi za anthu anu. Koma adzatsala mu mtsinje wa Nailo basi.” Onani mutuwoBuku Lopatulika11 Ndipo achule adzachokera inu, ndi nyumba zanu, ndi anyamata anu, ndi anthu anu; adzatsala m'mtsinje mokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo achule adzachokera inu, ndi nyumba zanu, ndi anyamata anu, ndi anthu anu; adzatsala m'nyanja mokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Achulewo adzakuchokani, adzachokanso m'nyumba zanu, m'nyumba za nduna zanu, ndipo azidzangokhala mumtsinje mokha.” Onani mutuwo |