Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 7:24 - Buku Lopatulika

24 Koma Aejipito onse anakumba m'mphepete mwa mtsinje kufuna madzi akumwa; pakuti sanakhoze kumwa madzi a m'mtsinjemo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Koma Aejipito onse anakumba m'mphepete mwa nyanja kufuna madzi akumwa; pakuti sanakhoze kumwa madzi a m'nyanjamo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Aejipito onse adayamba kukumba m'mbali mwa mtsinje wa Nailo kuti apeze madzi akumwa, chifukwa sankathanso kumwa madzi a mu mtsinjewo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Anthu onse a ku Igupto anayamba kukumba mʼmbali mwa mtsinje wa Nailo kuti apeze madzi akumwa, chifukwa sanathe kumwa madzi a mu mtsinjemo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 7:24
3 Mawu Ofanana  

Ndi nsomba zili m'mtsinje zidzafa, ndi mtsinje idzanunkha; ndi Aejipito adzachita mtima useru ndi kumwa madzi a m'mtsinjemo.


Ndipo Farao anatembenuka, nalowa m'nyumba yake, osasamalira ichi chomwe mumtima mwake.


Ndipo anafikira masiku asanu ndi awiri atapanda mtsinje Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa