Eksodo 5:5 - Buku Lopatulika5 Farao anatinso, Taonani, anthu a m'dziko ndiwo ambiri tsopano; ndipo inu muwapumitsa ku akatundu ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Farao anatinso, Taonani, anthu a m'dziko ndiwo ambiri tsopano; ndipo inu muwapumitsa ku akatundu ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Farao adapitirira kuŵauza kuti, “Anthu ameneŵa akuchulukana kwambiri tsopano. Bwanji inu mufuna kuŵaletsa kugwira ntchito yao?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndiponso Farao anati, “Taonani, anthuwa mʼdziko muno alipo ochuluka, ndipo inu mukuwaletsa kugwira ntchito.” Onani mutuwo |