Eksodo 5:22 - Buku Lopatulika22 Pamenepo Mose anabwerera nanka kwa Yehova, nati, Ambuye, mwawachitiranji choipa anthuwa? Mwandituma bwanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pamenepo Mose anabwerera namka kwa Yehova, nati, Ambuye, mwawachitiranji choipa anthuwa? Mwandituma bwanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Choncho Mose adapemphera kwa Chauta nati, “Inu Chauta, chifukwa chiyani mukuzunza anthu anu? Nanga ine mudanditumiranji? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Mose anabwerera kwa Yehova ndipo anati, “Chonde Ambuye, chifukwa chiyani mukuzunza anthu anu? Kodi munanditumira zimenezi? Onani mutuwo |