Eksodo 4:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo tsopano muka, ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi kukuphunzitsa chomwe ukalankhule. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo tsopano muka, ndipo Ine ndidzakhala m'kamwa mwako, ndi kukuphunzitsa chomwe ukalankhule. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono pita, Ine ndidzakuthandiza kulankhulako, ndipo zoti ukanene ndidzakuuza ndine.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Tsopano pita, Ine ndidzakuthandiza kuyankhula ndipo ndidzakulangiza zoti ukanene.” Onani mutuwo |