Eksodo 39:43 - Buku Lopatulika43 Ndipo Mose anaona ntchito zonse, ndipo, taonani, adaichita monga Yehova adamuuza, momwemo adachita. Ndipo Mose anawadalitsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Ndipo Mose anaona ntchito zonse, ndipo, taonani, adaichita monga Yehova adamuuza, momwemo adachita. Ndipo Mose anawadalitsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsono Mose adaona zonse zimene zidapangidwazo, ndipo adatsimikiza kuti adazipangadi monga momwe Chauta adalamulira. Pamenepo Mose adaŵadalitsa anthu onsewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Mose anayendera ntchitoyo ndipo anaona kuti anayichita monga momwe Yehova analamulira. Kotero Mose anawadalitsa. Onani mutuwo |