Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 39:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo anapanga miliu ya golide woona, napakiza miliu ndi makangaza, pa mkawo wa mwinjiro pozungulira, popakiza ndi makangaza.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo anapanga miliu ya golide woona, napakiza miliu ndi makangaza, pa mkawo wa mwinjiro pozungulira, popakiza ndi makangaza.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Adapanganso timabelu ta golide wabwino kwambiri, mopakiza pakati pa makangazawo, kuzungulira mpendero wonse wam'munsiwo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Ndipo anapanga maberu agolide wabwino kwambiri ndipo analumikiza mozungulira mpendero pakati pa makangadzawo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 39:25
5 Mawu Ofanana  

Odala anthu odziwa liu la lipenga; ayenda m'kuunika kwa nkhope yanu, Yehova.


Napangira pa mkawo wa mwinjiro makangaza a lamadzi, ndi lofiirira, ndi lofiira, ndi bafuta wa thonje losansitsa.


Mliu ndi khangaza, mliu ndi khangaza pa mkawo wa mwinjiro pozungulira, kutumikira nazo; monga Yehova anamuuza Mose.


Mphukira zako ndi munda wamakangaza, ndi zipatso zofunika, bonongwe ndi narido.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa