Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 38:29 - Buku Lopatulika

29 Ndi mkuwa wa choperekacho ndiwo matalente makumi asanu ndi awiri, ndi masekeli zikwi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Ndi mkuwa wa choperekacho ndiwo matalente makumi asanu ndi awiri, ndi masekeli zikwi ziwiri kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Mkuŵa umene adaapereka kwa Chauta udakwana makilogaramu 2,425 pamodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Mkuwa ochokera ku nsembe yoweyula unali makilogalamu 2,425.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 38:29
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anapanga zokowera za mizati nsanamira ndi nsichi ndi masekeli aja chikwi chimodzi kudza mazana asanu ndi awiri mphambu asanu, nakuta mitu yake, nazigwirizanitsa pamodzi.


Ndipo anapanga nao makamwa a pa khomo la chihema chokomanako, ndi guwa la nsembe lamkuwa, ndi sefa wake amkuwa, ndi zipangizo zonse za guwa la nsembe,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa