Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 37:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide, kunyamulira nazo gomelo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo anapanga mphiko za mtengo wakasiya, nazikuta ndi golide, kunyamulira nazo gomelo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Adapanga mphiko za matabwa a mtengo wa kasiya, nazikuta ndi golide.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Anapanga nsichi zamtengo wa mkesha ndi kuzikuta ndi golide kuti azinyamulira tebulolo.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 37:15
3 Mawu Ofanana  

ndi zikopa za nkhosa zamphongo zonyika zofiira, ndi zikopa za akatumbu, ndi mtengo wakasiya;


Mphetezo zinali pafupi pa mitanda, zikhale zopisamo mphiko kunyamulira nazo gomelo.


Anapanganso zipangizo za gomelo, mbale zake, ndi zipande zake, ndi mitsuko yake, ndi zikho zake zakuthira nazo, za golide woona.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa