Eksodo 35:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Mose ananena ndi khamu lonse la ana a Israele, ndi kuti, Ichi ndi chimene Yehova analamula ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Mose ananena ndi khamu lonse la ana a Israele, ndi kuti, Ichi ndi chimene Yehova anauza ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mose adauza Aisraele onse aja kuti, “Chauta akukulamulani kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mose ananena kwa gulu lonse la Aisraeli kuti, “Zimene Yehova wakulamulirani ndi izi: Onani mutuwo |