Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 34:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo Mose anafulumira, naweramira pansi nalambira.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo Mose anafulumira, naweramira pansi nalambira.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Pamenepo Mose adagwada pansi napembedza.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Pamenepo Mose anawerama pansi napembedza.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 34:8
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Abramu anagwa nkhope pansi, ndipo Mulungu ananena naye kuti,


Ndipo Yosefe anatulutsa iwo pakati pa maondo ake, nawerama ndi nkhope yake pansi.


Ndipo Yehosafati anawerama mutu wake, nkhope yake pansi; ndi Ayuda onse, ndi okhala mu Yerusalemu anagwa pansi pamaso pa Yehova, nalambira Yehova.


Ndipo anthuwo anakhulupirira; ndipo pamene anamva kuti Yehova adawazonda ana a Israele, ndi kuti adaona mazunzo ao, anawerama, nalambira Mulungu.


monga momwe ndinapangana nanu muja munatuluka mu Ejipito, ndi Mzimu wanga unakhala pakati pa inu; musamaopa inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa