Eksodo 34:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Ulembere mau awa; pakuti monga mwa mau awa ndapangana ndi iwe ndi Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Ulembere mau awa; pakuti monga mwa mau awa ndapangana ndi iwe ndi Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Chauta adauzanso Mose kuti, “Lemba mauŵa, chifukwa potsata mau ameneŵa, ndikuchita chipangano ndi iwe ndi Aisraele onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Lemba mawu awa pakuti potsatira mawuwa, ine ndipangana pangano ndi iwe ndi Israeli.” Onani mutuwo |