Eksodo 34:14 - Buku Lopatulika14 pakuti musalambira mulungu wina; popeza Yehova dzina lake ndiye Wansanje, ali Mulungu wansanje; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 pakuti musalambira mulungu wina; popeza Yehova dzina lake ndiye Wansanje, ali Mulungu wansanje; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Musadzapembedze mulungu wina aliyense, chifukwa Chauta amene dzina lake ndi Kansanje, ndi Mulungu wansanjedi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Musapembedze mulungu wina, pakuti Yehova amene dzina lake ndi Nsanje, ndi Mulungu wa nsanje. Onani mutuwo |