Eksodo 34:12 - Buku Lopatulika12 Dzichenjere ungachite pangano ndi anthu a ku dziko limene umukako, lingakhale msampha pakati panu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Dzichenjere ungachite pangano ndi anthu a ku dziko limene umukako, lingakhale msampha pakati panu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Musamale kuti musachite chipangano ndi anthu a ku dziko limene mukupitakolo, kuwopa kuti chingadzakhale msampha wokuchimwitsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Musamale kuti musakachite mgwirizano ndi anthu amene akukhala mʼdziko limene mukupitalo, chifukwa mukadzatero iwo adzakhala ngati msampha pakati panu. Onani mutuwo |