Eksodo 33:20 - Buku Lopatulika20 Ananenanso, Sungathe kuona nkhope yanga; pakuti palibe munthu adzandiona Ine ndi kukhala ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ananenanso, Sungathe kuona nkhope yanga; pakuti palibe munthu adzandiona Ine ndi kukhala ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Chauta adaonjeza kuti, “Koma sungathe kuwona nkhope yanga, chifukwa palibe munthu angathe kundiwona Ine, nakhala moyo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Iye anati, “Koma iwe sungaone nkhope yanga, pakuti palibe munthu amene amaona Ine nakhala ndi moyo.” Onani mutuwo |