Eksodo 33:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo tsopano, ngati ndapeza ufulu pamaso panu, mundidziwitsetu njira zanu, kuti ndikudziweni, ndi kuti ndipeze ufulu pamaso panu; ndipo penyani kuti mtundu uwu ndi anthu anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo tsopano, ngati ndapeza ufulu pamaso panu, mundidziwitsetu njira zanu, kuti ndikudziweni, ndi kuti ndipeze ufulu pamaso panu; ndipo penyani kuti mtundu uwu ndi anthu anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Nchifukwa chake tsono ndikukupemphani kuti ngati mwandikomera mtima, mundilangize njira zanu kuti ndikudziŵeni ndipo mupitirize kundikomera mtima. Kumbukiraninso kuti mtundu wa anthu uwu ndi wanu ndithu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ngati mwakondwera nane ndiphunzitseni njira zanu kuti ndikudziweni ndi kupitiriza kupeza chisomo pamaso panu. Kumbukirani kuti mtundu uwu ndi anthu anu.” Onani mutuwo |