Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 32:3 - Buku Lopatulika

3 Ndipo anthu onse anathyola mphete zagolide zinali m'makutu mwao, nabwera nazo kwa Aroni

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Ndipo anthu onse anathyola mphete zagolide zinali m'makutu mwao, nabwera nazo kwa Aroni

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Anthuwo adavuladi nsapule zao, ndipo adabwera nazo kwa Aroni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Kotero anthu onse anavula ndolo zagolide ndi kubwera nazo kwa Aaroni.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 32:3
10 Mawu Ofanana  

Ndipo panali zitatha kumwa ngamira, munthuyo anatenga mphete yagolide ya kulemera kwake sekeli latheka, ndi zingwinjiri ziwiri za m'manja ake, kulemera kwake masekeli khumi a golide.


Ndipo anampatsa Yakobo milungu yachilendo yonse inali m'manja mwao, ndi mphete zinali m'makutu mwao: ndipo Yakobo anazibisa pansi pa mtengo wathundu unali pa Sekemu.


Ndipo Aroni ananena nao, Thyolani mphete zagolide zili m'makutu a akazi anu, a ana anu aamuna ndi aakazi, ndi kubwera nazo kwa ine.


Ndipo anazilandira ku manja ao, nachikonza ndi chozokotera, nachiyenga mwanawang'ombe; ndipo anati, Siyi milungu yako, Israele, imene inakukweza kuchokera m'dziko la Ejipito.


Ndipo ana a Israele anazichotsera zokometsera zao kuyambira paphiri la Horebu.


mbera, ndi makoza, ndi nsalu za pankhope;


Amene ataya golide, namtulutsa m'thumba, ndi kuyesa siliva ndi muyeso, iwo alemba wosula golide; iye napanga nazo mulungu; iwo agwada pansi, inde alambira.


Abwera ndi siliva wa ku Tarisisi, wosulasula wopyapyala ndi golide wa ku Ufazi, ntchito ya mmisiri ndi manja a woyenga; zovala zao ndi nsalu ya madzi ndi yofiirira; zonsezi ndi ntchito za muomba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa