Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 32:24 - Buku Lopatulika

24 Ndipo ndinanena nao, Aliyense ali naye golide amthyole; ndipo anandipatsa; ndipo ndinachiponya m'moto, ndimo anatulukamo mwanawang'ombe uyu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Ndipo ndinanena nao, Aliyense ali naye golide amthyole; ndipo anandipatsa; ndipo ndinachiponya m'moto, ndimo anatulukamo mwanawang'ombe uyu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Tsono ine ndidaŵauza kuti, ‘Aliyense amene ali ndi golide abwere naye.’ Ndipo amene anali nazo zinthu zopangidwa ndi golide adandipatsa. Ndidaziponya pa moto, ndipo ndidapanga fano la mwanawang'ombe lija.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Choncho ine ndinawawuza kuti, ‘Aliyense amene ali ndi zokometsera zagolide azivule.’ Choncho iwo anandipatsa golide, ndipo ndinamuponya pa moto ndi kupanga fano la mwana wangʼombeyu.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 32:24
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anakantha anthu, chifukwa anapanga mwanawang'ombe amene Aroni anapanga.


Ndipo anazilandira ku manja ao, nachikonza ndi chozokotera, nachiyenga mwanawang'ombe; ndipo anati, Siyi milungu yako, Israele, imene inakukweza kuchokera m'dziko la Ejipito.


Koma iye, pofuna kudziyesa yekha wolungama, anati kwa Yesu, Ndipo mnansi wanga ndani?


monga kwalembedwa, Palibe mmodzi wolungama, inde palibe mmodzi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa