Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 30:37 - Buku Lopatulika

37 Koma za chofukizacho uchikonze, musadzikonzere nokha china, mwa makonzedwe ake amene; muchiyese chopatulika cha Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

37 Koma za chofukizacho uchikonze, musadzikonzere nokha china, mwa makonzedwe ake amene; muchiyese chopatulika cha Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

37 Ndipo lubani amene upangeyo potsata mapangidwe ake, asadzakhalire inuyo ai, koma adzakhale woyera wokhalira Chauta yekha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

37 Musapange lubani wanu potsatira njira iyi. Lubani yense wopangidwa mwa njira iyi akhale wopatulika, woperekedwa kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 30:37
4 Mawu Ofanana  

Uchitire guwa la nsembe choteteza masiku asanu ndi awiri ndi kulipatula; ndipo guwa la nsembelo likhale lopatulika kwambiri; chilichonse chikhudza guwa la nsembelo chikhale chopatulika.


Aliyense wokonza china chotere kununkhizapo, achotsedwe kwa anthu a mtundu wake.


Ndipo chotsalira cha nsembe yaufa chikhale cha Aroni ndi ana ake; ndicho chopatulika kwambiri cha nsembe zamoto za Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa