Eksodo 30:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Udzitengere zonunkhira, natafi, ndi sekeleti, ndi kelebuna; zonunkhira pamodzi ndi lubani loona; miyeso yofanana; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo Yehova anati kwa Mose, Udzitengere zonunkhira, natafi, ndi sekeleti, ndi kelebuna; zonunkhira pamodzi ndi lubani loona; miyeso yofanana; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Tsono Chauta adauza Mose kuti, “Utenge miyeso yofanafana ya zonunkhira bwino izi: sitakate, onika, galibanumu, ndi lubani weniweni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Kenaka Yehova anati kwa Mose, “Tenga muyeso wofanana wa zinthu zonunkhira izi: sitakate, onika, galibanumu pamodzi ndi lubani weniweni. Onani mutuwo |