Eksodo 30:33 - Buku Lopatulika33 Aliyense amene akonza ena otere, kapena aliyense awaika pa mlendo, ameneyo asazidwe kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Aliyense amene akonza ena otere, kapena aliyense awaika pa mlendo, ameneyo asazidwe kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Munthu aliyense amene adzapange mafuta ena ofanafana nawo, kapena kudzozera munthu aliyense amene sali wansembe, adzamchotsa pakati pa anthu anzake.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Wina aliyense amene adzapanga mafuta wonunkhira wofanana nawo kapena kudzozera mafutawa munthu wamba osati wansembe ayenera kuchotsedwa pakati pa anthu anzake.” Onani mutuwo |