Eksodo 30:30 - Buku Lopatulika30 Ndipo udzoze Aroni ndi ana ake aamuna, ndi kuwapatula andichitire ntchito ya nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Ndipo udzoze Aroni ndi ana ake amuna, ndi kuwapatula andichitire ntchito ya nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Kenaka udzamdzoze Aroni pamodzi ndi ana ake, ndi kuŵapatula kuti akhale ansembe onditumikira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 “Udzoze Aaroni ndi ana ake aamuna ndi kuwapatula kuti akhale ansembe onditumikira. Onani mutuwo |