Eksodo 3:19 - Buku Lopatulika19 Koma Ine ndidziwa kuti mfumu ya Aejipito siidzalola inu kumuka, inde lingakhale ndi dzanja lamphamvu ai. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Koma Ine ndidziwa kuti mfumu ya Aejipito siidzalola inu kumuka, inde lingakhale ndi dzanja lamphamvu ai. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Kudziŵa ndikudziŵa kuti mfumu ya ku Ejipitoyo sidzakulolani kuti mupite, mpaka nditaikakamiza kutero. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Koma Ine ndikudziwa kuti mfumu ya Igupto sikakulolani kuti mupite pokhapokha Ine nditayikakamiza. Onani mutuwo |