Eksodo 29:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ubwere nao Aroni ndi ana ake aamuna ku khomo la chihema chokomanako, ndi kuwasambitsa m'madzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ubwere nao Aroni ndi ana ake amuna ku khomo la chihema chokomanako, ndi kuwasambitsa m'madzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ubwere naye Aroni ku khomo la chihema chamsonkhano, pamodzi ndi ana ake aamuna, ndipo onsewo uŵayeretse m'madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kenaka ubwere naye Aaroni ndi ana ake pa khomo la tenti ya msonkhano ndipo uwasambitse ndi madzi. Onani mutuwo |