Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 29:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo utenge nkhosa yamphongo yodzaza manja, nuphike nyama yake m'malo opatulika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo utenge nkhosa yamphongo yodzaza manja, nuphike nyama yake m'malo opatulika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 “Tsono utenge nkhosa yamphongo yophera mwambo woloŵera unsembe, uiphike m'malo oyera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 “Utenge nkhosa yayimuna ya pamwambo wodzoza ansembe ndipo uyiphike pamalo opatulika.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 29:31
8 Mawu Ofanana  

mwana wake wamwamuna amene adzakhala wansembe m'malo mwake azivala masiku asanu ndi awiri, pakulowa iye m'chihema chokomanako kutumikira m'malo opatulika.


Ndipo Aroni ndi ana ake aamuna adye nyama ya nkhosa yamphongoyo, ndi mkate uli mudengu, pa khomo la chihema chokomanako.


Pamenepo anati kwa ine, Zipinda za kumpoto, ndi zipinda za kumwera, zili chakuno cha mpatawo, ndizo zipinda zopatulika, kumene ansembe okhala pafupi pa Yehova azidyera zinthu zopatulika kwambiri; kumeneko aziika zopatulika kwambiri, ndi nsembe yaufa, ndi nsembe yauchimo, ndi nsembe yopalamula; pakuti malowo ndi opatulika.


Ndipo anabwera nayo nkhosa yamphongo yinayo, ndiyo mphongo ya kudzaza manja; ndipo Aroni ndi ana ake aamuna anaika manja ao pamutu wa mphongoyo.


Ndipo Mose anati kwa Aroni ndi kwa ana ake aamuna, Phikani nyamayi pakhomo pa chihema chokomanako; ndipo muidyere komweko ndi mkate uli mu dengu la nsembe zodzaza manja, monga ndinauza, ndi kuti, Aroni ndi ana ake aidye.


Ndipo machitidwe a ansembe akuchitira anthu ndiwo, kuti pamene munthu aliyense akapereka nsembe, mnyamata wa wansembeyo akabwera, nyama ili chiwirire, ndi chovuulira cha ngowe cha mano atatu m'dzanja lake;


Ngakhale asanayambe kupsereza mafuta, amadza mnyamata wa wansembe, namuuza wopereka nsembe, nati, Umpatse wansembeyo nyama yoti akaotche; pakuti safuna nyama yako yophika koma yaiwisi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa