Eksodo 29:15 - Buku Lopatulika15 Utengenso nkhosa yamphongo imodziyo; ndi Aroni ndi ana ake aamuna aike manja ao pamutu pa nkhosa yamphongoyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Utengenso nkhosa yamphongo imodziyo; ndi Aroni ndi ana ake amuna aike manja ao pamutu pa nkhosa yamphongoyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 “Utenge imodzi mwa nkhosa ziŵiri zamphongo zija, ndipo Aroni ndi ana ake aamuna asanjike manja ao pamutu pa nkhosayo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 “Utenge nkhosa yayimuna imodzi ndipo Aaroni ndi ana ake aamuna asanjike manja awo pamutu pake. Onani mutuwo |