Eksodo 28:7 - Buku Lopatulika7 Akhale nazo zapamapewa ziwiri zomangika ku nsonga zake ziwiri, kuti amangike nazo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Akhale nazo zapamapewa ziwiri zomangika ku nsonga zake ziwiri, kuti amangike nazo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Idzakhale ndi tizikwewo tam'mapewa tiŵiri tosokerera ku nsonga zake ziŵiri, tomangira efodiyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Efodiyo ikhale ndi timalamba tiwiri ta pa mapewa tosokerera ku msonga zake ziwiri kuti azitha kumanga. Onani mutuwo |