Eksodo 28:36 - Buku Lopatulika36 Ndipo upange golide waphanthiphanthi woona, ndi kulochapo, monga malochedwe a chosindikizira, Kupatulikira Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201436 Ndipo upange golide waphanthiphanthi woona, ndi kulochapo, monga malochedwe a chosindikizira, Kupatulikira Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa36 “Upangenso duŵa la golide wabwino kwambiri, ulembepo mozokota mau akuti, ‘Choperekedwa kwa Chauta.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero36 “Upange duwa lagolide wabwino kwambiri kukhala ngati chidindo ndipo uzokotepo mawu akuti, choperekedwa kwa Yehova. Onani mutuwo |