Eksodo 28:34 - Buku Lopatulika34 mliu wa golide ndi khangaza, mliu wagolide ndi khangaza, pa mbinyiru wa mwinjiro pozungulira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 mliu wa golide ndi khangaza, mliu wagolide ndi khangaza, pa mbinyiru wa mwinjiro pozungulira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Choncho pakhale khangaza limodzi ndi kabelu kamodzi, khangaza limodzi ndi kabelu kamodzi, kuzungulira mpendero wonse wam'munsiwo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Choncho pazikhala mphonje imodzi kenaka belu limodzi, kuzungulira mpendero wa mkanjo wonse. Onani mutuwo |