Eksodo 27:17 - Buku Lopatulika17 Nsichi zonse za pabwalo pozungulira zimangike pamodzi ndi mitanda yasiliva; zokowera zao zasiliva, ndi makamwa ao amkuwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Nsichi zonse za pabwalo pozungulira zimangike pamodzi ndi mitanda yasiliva; zokowera zao zasiliva, ndi makamwa ao amkuwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Nsanamira zonse kuzungulira bwalolo zilumikizidwe ndi mitanda yasiliva, ndipo ngoŵe zake zikhalenso zasiliva, koma masinde ake akhale amkuŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mizati yonse yozungulira bwalolo ilumikizidwe ndi zingwe zasiliva. Ngowe zake zikhale zasiliva, koma matsinde ake akhale amkuwa. Onani mutuwo |