Eksodo 25:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo uzipanga chotetezerapo cha golide woona; utali wake mikono iwiri ndi hafu, ndi kupingasa kwake mkono ndi hafu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo uzipanga chotetezerapo cha golide woona; utali wake mikono iwiri ndi hafu, ndi kupingasa kwake mkono ndi hafu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “Upange ndi golide wabwino kwambiri chivundikiro cha bokosi, kutalika kwake masentimita 114, kupingasa kwake masentimita 69. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Upange chivundikiro cha bokosilo cha golide wabwino kwambiri, kutalika kwake masentimita 114, mulifupi mwake masentimita 69. Onani mutuwo |