Eksodo 24:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo Mose anagawa mwaziwo, nathira wina m'zotengera, nawaza wina paguwa la nsembe Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo Mose anagawa mwaziwo, nathira wina m'zotengera, nawaza wina pa guwa la nsembe Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mose adatengako theka la magazi, naŵathira m'mbale, ndipo magazi otsala adawaza pa guwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mose anatenga theka la magazi ndi kuyika mʼmbale, ndipo theka linalo analiwaza pa guwa lansembe. Onani mutuwo |
Pamenepo uiphe nkhosa yamphongoyo, nutapeko pa mwazi wake, ndi kuupaka pa ndewerere ya khutu lamanja la Aroni, ndi pa ndewerere ya khutu lamanja ana ake aamuna, ndi pa chala chachikulu cha dzanja lao lamanja, ndi pa chala chachikulu cha phazi lao lamanja ndi kuuwaza mwaziwo paguwa la nsembe posungulira.