Eksodo 23:28 - Buku Lopatulika28 Ndipo ndidzatumiza mavu akutsogolere amene adzaingitsa Ahivi, Akanani, ndi Ahiti, pamaso pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Ndipo ndidzatumiza mavu akutsogolere amene adzaingitsa Ahivi, Akanani, ndi Ahiti, pamaso pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Ndidzapirikitsa Ahivi, Akanani ndi Ahiti, inu musanafike, ndipo adzathaŵa monga ngati ndaŵatumira mavu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Ahivi, Akanaani ndi Ahiti adzathawa ngati kuti ndawatumizira mavu. Onani mutuwo |