Eksodo 23:14 - Buku Lopatulika14 Muzindichitira Ine madyerero katatu m'chaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Muzindichitira Ine madyerero katatu m'chaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 “Muzikhala ndi tsiku lachikondwerero katatu pa chaka, kuti mundilemekeze Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 “Muzichita zikondwerero zolemekeza Ine katatu pa chaka. Onani mutuwo |
Koma pofika anthu a m'dziko pamaso pa Yehova m'zikondwerero zoikika, iye amene alowera njira ya kuchipata cha kumpoto kudzalambira, atulukire njira ya kuchipata cha kumwera; ndi iye amene alowera njira ya kuchipata cha kumwera, atulukire njira ya kuchipata cha kumpoto; asabwerere njira ya chipata anadzeracho, koma atulukire m'tsogolo mwake.