Eksodo 22:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo usasautsa mlendo kapena kumpsinja; pakuti munali alendo m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo usasautsa mlendo kapena kumpsinja; pakuti munali alendo m'dziko la Ejipito. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Musazunze mlendo kapena kumkhalitsa m'phanthi, poti paja inunso munali alendo ku dziko la Ejipito. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Musazunze mlendo kapena kumuchitira nkhanza, pakuti inu munali alendo mʼdziko la Igupto. Onani mutuwo |