Eksodo 21:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo munthu akagulitsa mwana wake wamkazi akhale mdzakazi, iyeyu asatuluke monga amatuluka anyamata. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo munthu akagulitsa mwana wake wamkazi akhale mdzakazi, iyeyu asatuluke monga amatuluka anyamata. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 “Munthu akagulitsa mwana wake wamkazi ku ukapolo, mwanayo sadzaomboledwa monga m'mene amachitira ndi akapolo aamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Ngati munthu agulitsa mwana wake wamkazi kukhala mdzakazi, mwanayo asamasulidwe monga achitira ndi akapolo aamuna. Onani mutuwo |