Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 21:33 - Buku Lopatulika

33 Munthu akafukula dzenje, kapena akakumba dzenje, osalivundikira, ndipo ikagwamo ng'ombe kapena bulu,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

33 Munthu akafukula dzenje, kapena akakumba dzenje, osalivundikira, ndipo ikagwamo ng'ombe kapena bulu,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

33 “Munthu akasiya dzenje lapululu, kapena akakumba dzenje, koma osaphimbira, tsono ng'ombe kapena bulu nkugweramo,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

33 “Munthu akasiya dzenje lapululu kapena akakumba dzenje koma wosaphimbapo, ndipo ngʼombe kapena bulu nʼkugweramo,

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 21:33
9 Mawu Ofanana  

Odzikuza anandikumbira mbuna, ndiwo osasamalira chilamulo chanu.


Amitundu anagwa m'mbuna imene anaikumba, lakodwa phazi lao muukonde anautchera.


Ng'ombeyo ikatunga mnyamata kapena mdzakazi, azipatsa mbuye wake ndalama za masekeli a siliva makumi atatu, ndipo ng'ombeyo aiponye miyala.


mwini dzenje azilipa; azilipa ndalama kwa mwini nyamayo, koma yakufayo ndi yake.


Wosocheretsa oongoka mtima alowe m'njira yoipa, adzagwa mwini m'dzenje lake; koma angwiro adzalandira cholowa chabwino.


Wokumba mbuna adzagwamo; ndipo woboola mpanda njoka idzamluma.


Kodi choipa chibwezedwe pa chabwino? Pakuti akumbira moyo wanga dzenje. Mukumbukire kuti ndinaima pamaso panu kuwanenera zabwino, kuwachotsera iwo ukali wanu.


Mfuu umvekedwe m'nyumba zao, pamene muwatengera khamu la nkhondo dzidzidzi; pakuti akumba dzenje lakundigwira ine, anabisira mapazi anga misampha.


Munthu akakantha nyama kuti ife, ambwezere ina; moyo kulipa moyo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa