Eksodo 20:23 - Buku Lopatulika23 Musapange milungu yasiliva ikhale pamodzi ndi Ine; musadzipangire milungu yagolide. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Musapange milungu yasiliva ikhale pamodzi ndi Ine; musadzipangire milungu yagolide. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Musadzipangire milungu yasiliva kapena yagolide, kuti muziipembedzera kumodzi ndi Ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Choncho musadzipangire milungu yasiliva kapena yagolide kuti muziyipembedza pamodzi ndi Ine.’ ” Onani mutuwo |
koma munadzikweza kutsutsana naye Ambuye wa Kumwamba; ndipo anabwera nazo zotengera za nyumba yake kwa inu; ndi inu ndi akulu anu, akazi anu ndi akazi anu aang'ono, mwamweramo vinyo; mwalemekezanso milungu yasiliva, ndi yagolide, yamkuwa, yachitsulo, yamtengo, ndi yamwala, imene siiona kapena kumva, kapena kudziwa; ndi Mulungu amene m'dzanja mwake muli mpweya wanu, ndi njira zanu zonse, yemweyo simunamchitire ulemu.