Eksodo 19:13 - Buku Lopatulika13 dzanja lililonse lisalikhudze, wakulikhudza azimponyatu miyala, kapena kumpyoza; ngakhale choweta ngakhale munthu, zisakhale ndi moyo. Pamene lipenga libanika liu lake azikwera m'phirimo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 dzanja lililonse lisalikhudze, wakulikhudza azimponyatu miyala, kapena kumpyoza; ngakhale choweta ngakhale munthu, zisakhale ndi moyo. Pamene lipenga libanika liu lake azikwera m'phirimo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Wina aliyense asakhudze munthuyo, koma anthu amponye miyala kapena kumubaya. Chikhale choŵeta, chidzaphedwa; akhale munthu, adzaphedwanso. Mbetete ikamalira, anthu abwere ku phiri.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Aliyense wokhudza phiri adzaphedwa ndi miyala kapena kumulasa ndi mivi. Palibe amene adzamukhudze. Palibe munthu amene adzaloledwa kukhala ndi moyo ngakhale nyama. Iwo adzayenera kuphedwa.’ Koma anthu adzapita ku phirilo akadzamva kulira kwa lipenga la nyanga yankhosa.” Onani mutuwo |