Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 16:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo kudzakhala tsiku lachisanu ndi chimodzi, kuti azikonza umene adabwera nao, ataonjezapo muyeso unzake wa pa tsiku limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo kudzakhala tsiku lachisanu ndi chimodzi, kuti azikonza umene adabwera nao, ataonjezapo muyeso unzake wa pa tsiku limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Pa tsiku lachisanu ndi chimodzi, pokonza chimene adatola adzapeza kuti nchokwanira masiku aŵiri.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Pa tsiku lachisanu ndi chimodzi, pamene azidzakonza buledi amene abwera naye, adzapeza kuti ndi wokwanira masiku awiri.”

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 16:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose ndi Aroni ananena ndi ana onse a Israele, Madzulo mudzadziwa kuti Yehova anakutulutsani m'dziko la Ejipito;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa