Eksodo 15:10 - Buku Lopatulika10 Munaombetsa mphepo yanu, nyanja inawamiza; anamira m'madzi aakulu ngati mtovu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Munaombetsa mphepo yanu, nyanja inawamiza; anamira m'madzi aakulu ngati mtovu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Koma Inu mudangouzira ndi mphepo yanu, ndipo nyanja idaŵamiza. Adangomira ngati chitsulo mpaka pansi pa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Koma Inu munawuzira mphepo yanu, ndipo nyanja inawaphimba. Iwo anamira ngati chitsulo mʼmadzi amphamvu. Onani mutuwo |