Eksodo 14:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ndidzalimbitsa mtima wake wa Farao kuti awalondole; ndipo ndidzalemekezedwa pa Farao ndi pa nkhondo yake yonse; pamenepo Aejipito adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndipo anachita chomwecho. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ndidzalimbitsa mtima wake wa Farao kuti awalondole; ndipo ndidzalemekezedwa pa Farao ndi pa nkhondo yake yonse; pamenepo Aejipito adzadziwa kuti Ine ndine Yehova, ndipo anachita chomwecho. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndidzamuumitsa mtima Farao, ndipo adzalondola Aisraelewo. Tsono ndikadzagonjetsa Farao pamodzi ndi gulu lonse lankhondo, ndidzalandira ulemu, ndipo Aejipito onse adzadziŵa kuti Ine ndine Chauta.” Choncho Aisraele adachita zonse monga momwe adaŵauzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ndidzawumitsa mtima wa Farao ndipo adzathamangira Aisraeliwo. Choncho ndikadzagonjetsa Farao ndi gulu lake lonse la nkhondo, Ine ndidzalemekezedwa.” Choncho Aisraeli aja anachita zimenezi. Onani mutuwo |