Eksodo 14:16 - Buku Lopatulika16 Ndipo iwe nyamula ndodo yako, nutambasulire dzanja lako kunyanja, nuigawe, kuti ana a Israele alowe pakati pa nyanja pouma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndipo iwe nyamula ndodo yako, nutambasulire dzanja lako kunyanja, nuigawe, kuti ana a Israele alowe pakati pa nyanja pouma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Tenga ndodo yakoyo, ndipo utambalitse dzanja pa nyanja, kuigaŵa nyanjayo kuti Aisraele aoloke pouma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Nyamula ndodo yako ndi kutambasula dzanja lako kuloza ku nyanja, kugawa madzi kuti Aisraeli awoloke powuma. Onani mutuwo |