Eksodo 13:18 - Buku Lopatulika18 Koma Mulungu anawazungulitsa anthuwo, ku njira ya kuchipululu ya Nyanja Yofiira; ndipo ana a Israele anakwera kuchokera m'dziko la Ejipito okonzeka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Mulungu anawazungulitsa anthuwo, ku njira ya kuchipululu ya Nyanja Yofiira; ndipo ana a Israele anakwera kuchokera m'dziko la Ejipito okonzeka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 M'malo mwake Mulungu adaŵadzeretsa njira yozungulira, yachipululu, yopita ku Nyanja Yofiira. Monsemo nkuti Aisraele ali okonzekeratu za nkhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Choncho Mulungu anawadzeretsa anthuwo njira yozungulira ya mʼchipululu kulowera ku Nyanja Yofiira. Komabe Aisraeli anatuluka mʼdziko la Igupto atakonzekera nkhondo. Onani mutuwo |