Eksodo 12:32 - Buku Lopatulika32 Muka nazoni zoweta zanu zazing'ono ndi zazikulu, monga mwanena; chokani, ndi kundidalitsa inenso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Muka nazoni zoweta zanu zazing'ono ndi zazikulu, monga mwanena; chokani, ndi kundidalitsa inenso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Mutenge nkhosa zanu, mbuzi zanu ndi ng'ombe zanu zomwe, monga momwe mudanenera, ndipo muchoke. Mukapemphere kuti nanenso andidalitseko.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Tengani ziweto ndi ngʼombe zanu ndipo pitani kapembedzeni Mulungu wanu monga munanenera kuti ine ndidalitsike.” Onani mutuwo |