Eksodo 12:26 - Buku Lopatulika26 Ndipo kudzakhala, pamene ana anu adzanena ndi inu, Kutumikiraku muli nako nkutani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Ndipo kudzakhala, pamene ana anu adzanena ndi inu, Kutumikiraku muli nako nkutani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ana anu azidzakufunsani kuti, ‘Kodi mwambo umenewu umatanthauza chiyani?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndipo ana anu akakakufunsani kuti, ‘Mwambo umenewu ukutanthauza chiyani?’ Onani mutuwo |