Eksodo 12:24 - Buku Lopatulika24 Ndipo muzisunga chinthu ichi chikhale lemba la kwa inu, ndi kwa ana anu ku nthawi zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Ndipo muzisunga chinthu ichi chikhale lemba la kwa inu, ndi kwa ana anu ku nthawi zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Muziŵamvera malamulo ameneŵa inuyo ndi ana anu mpaka muyaya. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 “Muzimvera malamulo amenewa kwa muyaya, inu ndi zidzukulu zanu. Onani mutuwo |