Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Eksodo 10:11 - Buku Lopatulika

11 Chotero ai, mukani tsopano, inu amuna aakulu, tumikirani Yehova pakuti ichi muchifuna. Ndipo anawapirikitsa pamaso pa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Chotero ai, mukani tsopano, inu amuna akulu, tumikirani Yehova pakuti ichi muchifuna. Ndipo anawapirikitsa pamaso pa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Ai! Inu, amuna nokhanu, ndiye mupite mukapembedze Chauta, popeza kuti ndi zimene mukufuna.” Atangomveka mau ameneŵa, Mose ndi Aroni adapirikitsidwa pamaso pa Farao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ndakana! Amuna okha ndiwo apite ndi kukapembedza Yehova pakuti izi ndi zimene mwakhala mukupempha.” Kenaka Mose ndi Aaroni anathamangitsidwa pamaso pa Farao.

Onani mutuwo Koperani




Eksodo 10:11
5 Mawu Ofanana  

Odzikuza anandipangira bodza: Ndidzasunga malangizo anu ndi mtima wanga wonse.


Ndipo ananena nao, Momwemo, Yehova akhale nanu ngati ndilola inu ndi ana aang'ono anu mumuke; chenjerani pakuti pali choipa pamaso panu.


Ndipo Farao ananena naye, Choka pano, uzichenjera usaonenso nkhope yanga; pakuti tsiku limene uonanso nkhope yanga udzafa.


Ndipo mfumu ya Aejipito inanena nao, Inu, Mose ndi Aroni, chifukwa ninji mumasulira anthu ntchito zao? Mukani ku akatundu anu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa